Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 18:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Yonatani ndi Davide anachita pangano,+ chifukwa Yonatani anali kukonda Davide ngati mmene anali kudzikondera.+

  • 1 Samueli 20:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Pamenepo Yonatani anauza Davide kuti: “Pita mu mtendere,+ pakuti tonse awiri talumbira+ m’dzina la Yehova kuti, ‘Yehova akhale pakati pa iwe ndi ine, ndi pakati pa ana ako ndi ana anga mpaka kalekale.’”+

      Chotero Davide ananyamuka ndi kupita, koma Yonatani anabwerera kumzinda.

  • 1 Samueli 22:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Pakuti nonsenu mwandikonzera chiwembu chifukwa palibe aliyense amene anaulula kwa ine+ pamene mwana wanga anachita pangano+ ndi mwana wa Jese. Palibenso aliyense wa inu amene wandimvera chifundo ndi kuulula kwa ine kuti mwana wanga weniweni wasandutsa mtumiki wanga kukhala wondibisalira kuti andichite chiwembu monga mmene zililimu.”

  • 2 Samueli 21:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma mfumu inamvera chisoni Mefiboseti+ mwana wamwamuna wa Yonatani, mwana wa Sauli, chifukwa cha lumbiro+ limene Davideyo ndi Yonatani mwana wa Sauli anachita pakati pawo pamaso pa Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena