Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 20:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ukatero undisonyeze kukoma mtima kosatha ine mtumiki wako,+ pakuti unandilowetsa m’pangano+ la Yehova pamodzi ndi iwe. Koma ngati ndili wolakwa,+ undiphe ndiwe, m’malo moti uchite kukandipereka kwa bambo ako.”

  • 1 Samueli 20:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Pamenepo Yonatani anauza Davide kuti: “Pita mu mtendere,+ pakuti tonse awiri talumbira+ m’dzina la Yehova kuti, ‘Yehova akhale pakati pa iwe ndi ine, ndi pakati pa ana ako ndi ana anga mpaka kalekale.’”+

      Chotero Davide ananyamuka ndi kupita, koma Yonatani anabwerera kumzinda.

  • 1 Samueli 23:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Kenako awiriwo anachita pangano+ pamaso pa Yehova. Zitatero, Davide anapitiriza kukhala ku Horesi koma Yonatani anabwerera kwawo.

  • 2 Samueli 9:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndiyeno Davide ananena kuti: “Kodi pali aliyense wotsala wa m’nyumba ya Sauli? Ndikufuna kumusonyeza kukoma mtima kosatha+ chifukwa cha Yonatani.”+

  • 2 Samueli 21:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma mfumu inamvera chisoni Mefiboseti+ mwana wamwamuna wa Yonatani, mwana wa Sauli, chifukwa cha lumbiro+ limene Davideyo ndi Yonatani mwana wa Sauli anachita pakati pawo pamaso pa Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena