Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 23:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Uzikhalanso ndi chokumbira pamodzi ndi zida zako. Ndiyeno podzithandiza kunja kwa msasa, uzikumba dzenje ndi chokumbiracho ndipo ukamaliza kudzithandiza uzitembenuka ndi kufotsera zoipazo.+

  • Oweruza 3:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 iyeyo n’kutuluka panja.+

      Pamenepo atumiki a Egiloni anafika n’kuyamba kuyang’ana, ndipo anapeza zitseko za chipinda cha padenga zili zokhoma. Ndiyeno anati: “Ayenera kuti akudzithandiza+ m’chipinda chozizira bwino cha mkatikati.”

  • 1 Mafumu 18:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Pofika masana Eliya anayamba kuwaseka+ ndipo anali kunena kuti: “Muitaneni mokuwa kwambiri chifukwa iye ndi mulungu.+ Mwina watanganidwa ndi zinazake, kapena wapita kuchimbudzi.+ Mwinanso wagona, ndipo muyenera kum’dzutsa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena