Genesis 18:33 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 33 Ndiyeno Yehova+ atamaliza kulankhula ndi Abulahamu, ananyamuka n’kumapita, ndipo Abulahamu anabwerera kunyumba kwake. Numeri 24:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Tsopano Balamu ananyamuka kumabwerera kwawo.+ Nayenso Balaki ananyamuka kulowera njira yake. 1 Samueli 24:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Zitatero, Davide analumbirira Sauli. Kenako Sauliyo anapita kwawo,+ koma Davide ndi amuna amene anali kuyenda naye anapita kumalo ovuta kufikako.+ 1 Samueli 27:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Patapita nthawi, uthenga unafika kwa Sauli wonena kuti Davide anathawira ku Gati. Atamva zimenezo sanapitenso kukam’sakasaka.+ 2 Samueli 19:39 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 39 Tsopano anthu onse anayamba kuwoloka Yorodano, ndipo mfumu nayonso inawoloka. Koma mfumu inapsompsona+ Barizilai ndi kumudalitsa,+ kenako Barizilai anabwerera kwawo.
33 Ndiyeno Yehova+ atamaliza kulankhula ndi Abulahamu, ananyamuka n’kumapita, ndipo Abulahamu anabwerera kunyumba kwake.
22 Zitatero, Davide analumbirira Sauli. Kenako Sauliyo anapita kwawo,+ koma Davide ndi amuna amene anali kuyenda naye anapita kumalo ovuta kufikako.+
4 Patapita nthawi, uthenga unafika kwa Sauli wonena kuti Davide anathawira ku Gati. Atamva zimenezo sanapitenso kukam’sakasaka.+
39 Tsopano anthu onse anayamba kuwoloka Yorodano, ndipo mfumu nayonso inawoloka. Koma mfumu inapsompsona+ Barizilai ndi kumudalitsa,+ kenako Barizilai anabwerera kwawo.