Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 31:55
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 55 Ndiyeno Labani anadzuka m’mamawa n’kupsompsona+ adzukulu ake ndi ana ake aakazi ndipo anawadalitsa.+ Atatero, ananyamuka kubwerera kwawo.+

  • Rute 1:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Atatero iwo analiranso mokweza mawu. Kenako Olipa anapsompsona apongozi ake powatsanzika. Koma Rute anawaumirirabe.+

  • 1 Samueli 20:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Mtumikiyo anapitadi. Zitatero, Davide anatulukira pafupi, chakum’mwera. Ndiyeno anagwada ndi kugunditsa nkhope yake pansi+ n’kuwerama katatu. Atatero, anayamba kupsompsonana+ ndi kulirirana mpaka Davide analira kwambiri kuposa Yonatani.+

  • 1 Mafumu 19:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Zitatero, Elisa anasiya ng’ombe zamphongozo n’kuthamangira Eliya ndipo anamuuza kuti: “Ndiloleni ndipite ndikapsompsone kaye bambo anga ndi mayi anga,+ kenako ndidzakutsatirani.” Eliya anamuyankha kuti: “Pita, sindingakuletse.”

  • Machitidwe 20:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Pamenepo onse analira kwambiri, ndipo anakumbatira+ Paulo ndi kumupsompsona mwachikondi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena