Genesis 29:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Tsopano Labani atangomva za Yakobo, mwana wa mlongo wake, anathamanga kukakumana naye.+ Atafika, anam’kumbatira ndi kum’psompsona, n’kupita naye kunyumba kwake.+ Kumeneko, Yakobo anafotokozera Labani zinthu zonse. Genesis 45:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Pamenepo Yosefe anayamba kupsompsona abale ake onsewo n’kumalira akuwakumbatira.+ Pambuyo pake, abale akewo analankhula naye. 1 Samueli 10:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Ndiyeno Samueli anatenga+ botolo ladothi la mafuta ndi kutsanulira mafutawo pamutu wa Sauli, n’kumupsompsona+ ndi kunena kuti: “Yehova wakudzoza iwe kukhala mtsogoleri+ wa cholowa chake.+ 2 Samueli 19:39 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 39 Tsopano anthu onse anayamba kuwoloka Yorodano, ndipo mfumu nayonso inawoloka. Koma mfumu inapsompsona+ Barizilai ndi kumudalitsa,+ kenako Barizilai anabwerera kwawo. Machitidwe 20:37 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 37 Pamenepo onse analira kwambiri, ndipo anakumbatira+ Paulo ndi kumupsompsona mwachikondi.+
13 Tsopano Labani atangomva za Yakobo, mwana wa mlongo wake, anathamanga kukakumana naye.+ Atafika, anam’kumbatira ndi kum’psompsona, n’kupita naye kunyumba kwake.+ Kumeneko, Yakobo anafotokozera Labani zinthu zonse.
15 Pamenepo Yosefe anayamba kupsompsona abale ake onsewo n’kumalira akuwakumbatira.+ Pambuyo pake, abale akewo analankhula naye.
10 Ndiyeno Samueli anatenga+ botolo ladothi la mafuta ndi kutsanulira mafutawo pamutu wa Sauli, n’kumupsompsona+ ndi kunena kuti: “Yehova wakudzoza iwe kukhala mtsogoleri+ wa cholowa chake.+
39 Tsopano anthu onse anayamba kuwoloka Yorodano, ndipo mfumu nayonso inawoloka. Koma mfumu inapsompsona+ Barizilai ndi kumudalitsa,+ kenako Barizilai anabwerera kwawo.