Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 6:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Uziopa Yehova Mulungu wako+ ndi kum’tumikira,+ ndipo uzilumbira pa dzina lake.+

  • Yoswa 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Tsopano, chonde lumbirani kwa ine pali Yehova,+ kuti chifukwa choti ndakusonyezani kukoma mtima kosatha, inunso mudzasonyeza anthu a m’nyumba ya bambo anga+ kukoma mtima kosatha, ndipo mundipatse chizindikiro chodalirika.+

  • Yoswa 9:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Choncho Yoswa anagwirizana nawo za mtendere,+ ndipo anachita nawo pangano kuti asawaphe. Zitatero, atsogoleri+ a Isiraeli analumbira kwa anthuwo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena