Genesis 21:33 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 33 Zitatero, Abulahamu anabzala mtengo wa bwemba pa Beere-seba, n’kuitanirapo dzina la Yehova,+ Mulungu wanthawi zonse.+ 1 Samueli 22:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Ndiyeno Sauli anamva kuti Davide ndi anthu amene anali naye apezeka. Iye anamva zimenezi ali ku Gibeya pamalo okwezeka, atakhala pansi pa mtengo wa bwemba.+ Sauliyo anali atagwira mkondo+ m’manja mwake ndipo atumiki ake onse anali atamuzungulira. 1 Mbiri 10:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Chotero amuna onse olimba mtima ananyamuka n’kukanyamula mtembo wa Sauli ndi mitembo ya ana ake n’kupita nayo ku Yabesi. Atatero anakafotsera mafupa awo pansi pa mtengo waukulu+ ku Yabesiko.+ Kenako anasala kudya+ masiku 7.
33 Zitatero, Abulahamu anabzala mtengo wa bwemba pa Beere-seba, n’kuitanirapo dzina la Yehova,+ Mulungu wanthawi zonse.+
6 Ndiyeno Sauli anamva kuti Davide ndi anthu amene anali naye apezeka. Iye anamva zimenezi ali ku Gibeya pamalo okwezeka, atakhala pansi pa mtengo wa bwemba.+ Sauliyo anali atagwira mkondo+ m’manja mwake ndipo atumiki ake onse anali atamuzungulira.
12 Chotero amuna onse olimba mtima ananyamuka n’kukanyamula mtembo wa Sauli ndi mitembo ya ana ake n’kupita nayo ku Yabesi. Atatero anakafotsera mafupa awo pansi pa mtengo waukulu+ ku Yabesiko.+ Kenako anasala kudya+ masiku 7.