Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ngakhalenso likasa la Mulungu linalandidwa,+ ndipo Hofeni ndi Pinihasi, ana awiri a Eli, anafa.+

  • Salimo 78:61
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 61 Analola kuti chizindikiro cha mphamvu zake chitengedwe ndi adani ake,+

      Iye analola kuti chizindikiro cha kukongola kwake chikhale m’manja mwa adani.+

  • Maliro 2:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Yehova wachita zimene anali kuganiza.+ Wakwaniritsa zimene ananena,+

      Zimene analamula kalekale.+ Wapasula zinthu ndipo sanamve chisoni.+

      Wachititsa adani ako kusangalala+ chifukwa cha zimene zakuchitikira. Wakweza nyanga ya adani+ ako.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena