-
Mateyu 2:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 Tsopano atalowa m’nyumbamo, anaona mwanayo ndi mayi ake Mariya. Choncho anagwada ndi kumuweramira. Kenako anamasula chuma chawo ndi kupereka kwa mwanayo mphatso za golide, lubani ndi mule.
-