Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 9:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ndiyeno Mulungu analola kuti pakhale kusamvana+ pakati pa Abimeleki ndi nzika za Sekemu, moti nzika za Sekemu zinayamba kuchitira Abimeleki zachinyengo.+

  • 1 Samueli 16:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Tsopano mzimu wa Yehova unachoka+ pa Sauli, ndipo Yehova analola maganizo oipa*+ kum’vutitsa Sauli.

  • 1 Samueli 19:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndiyeno mzimu woipa wa Yehova+ unayamba kugwira ntchito pa Sauli ali m’nyumba mwake, atatenga mkondo m’manja mwake. Pa nthawiyi, Davide anali kumuimbira nyimbo.

  • Yobu 34:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndithudi, Mulungu sachita zoipa,+

      Ndipo Wamphamvuyonse sakhotetsa chilungamo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena