Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 15:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Pamenepo mfumu inapitiriza kuuza Zadoki wansembe kuti: “Iwe ndi wamasomphenya,*+ si choncho kodi? Bwerera kumzinda mu mtendere. Bwerera pamodzi ndi Ahimazi mwana wako wamwamuna ndi Yonatani+ mwana wamwamuna wa Abiyatara. Mubwerere ndi ana anu awiri amene muli nawowa.

  • 2 Samueli 17:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pambuyo pake Husai anauza Zadoki+ ndi Abiyatara ansembe, kuti: “Ahitofeli wapereka malangizo kwa Abisalomu ndi akulu a Isiraeli ndipo wanena zakutizakuti, koma malangizo amene ine ndapereka, ndanena zakutizakuti.

  • 1 Mafumu 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Benaya+ mwana wa Yehoyada anali mkulu wa asilikali,+ ndipo Zadoki ndi Abiyatara+ anali ansembe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena