Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 6:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “Tsopano amenewa ndiwo malamulo, malangizo ndi zigamulo zimene Yehova Mulungu wanu walamula kuti ndikuphunzitseni,+ kuti muzikazitsatira m’dziko limene mukuwolokerako kukalitenga kukhala lanu.

  • Deuteronomo 7:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 “Ndiyeno mukapitiriza kumvera zigamulo zimenezi ndi kuzisunga,+ Yehova Mulungu wanu adzasunga pangano+ ndi kukusonyezani kukoma mtima kosatha, zimene analumbirira makolo anu.+

  • Salimo 19:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Kuopa+ Yehova n’koyera, ndipo kudzakhalapo kwamuyaya.

      Zigamulo+ za Yehova n’zolondola,+ ndipo pa mbali iliyonse zasonyezadi kuti ndi zolungama.+

  • Salimo 119:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  30 Ine ndasankha kuyenda mokhulupirika.+

      Zigamulo zanu ndimaziona kukhala zoyenera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena