Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 16:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pamapeto pake Samueli anafunsa Jese kuti: “Kodi anyamata ako onse ndi omwewa basi?” Iye anayankha kuti: “Wamng’ono kwambiri sanabwerebe,+ pakuti akuweta nkhosa.”+ Chotero Samueli anauza Jese kuti: “Tumiza munthu akam’tenge, chifukwa sitikhala pansi kuti tidye kufikira iye atabwera pano.”

  • 1 Mbiri 17:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Tsopano mtumiki wanga Davide ukamuuze kuti, ‘Yehova wa makamu wanena kuti: “Ine ndinakutenga kubusa kumene unali kusamalira nkhosa+ kuti ukhale mtsogoleri+ wa anthu anga Aisiraeli.

  • Salimo 78:70
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 70 Choncho anasankha Davide mtumiki wake,+

      Ndipo anamuchotsa kumakola a nkhosa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena