Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 3:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Choncho Samueli anamuuza mawu onse ndipo sanam’bisire kanthu. Pamenepo Eli anati: “Ndi Yehova amene wanena. Achite zimene akuona kuti n’zabwino.”+

  • 1 Samueli 14:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Choncho Yonatani anauza mtumiki wake womunyamulira zida uja kuti: “Tiye tiwolokere kumudzi wa amuna osadulidwawa.+ Pakuti mwina Yehova adzatithandiza, chifukwa palibe chimene chingalepheretse Yehova kupulumutsa anthu ake pogwiritsa ntchito anthu ambiri kapena ochepa.”+

  • 2 Samueli 15:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Koma akanena kuti, ‘Sindikusangalala nawe,’ ine ndidzavomereza zilizonse zimene adzandichitira.”+

  • Salimo 37:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Lola kuti Yehova akutsogolere panjira yako,+

      Umudalire+ ndipo iye adzachitapo kanthu.+

  • Salimo 44:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ndi thandizo lanu tidzakankha adani athu.+

      M’dzina lanu tidzapondereza amene akutiukira.+

  • Miyambo 29:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Kuopa anthu n’kumene kumatchera msampha,+ koma wokhulupirira Yehova adzatetezedwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena