Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 4:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Tsopano mwamuna wina wa fuko la Benjamini anathamanga kuchoka kumalo ankhondowo kukafika ku Silo tsiku limenelo, atang’amba zovala zake+ ndi kudzithira dothi kumutu.+

  • 2 Samueli 1:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno pa tsiku lachitatu anaona munthu wina+ akubwera kuchokera kumsasa, kwa Sauli. Iye anali atang’amba zovala zake+ komanso atadzithira dothi kumutu.+ Atafika kwa Davide, nthawi yomweyo anagwada ndi kuwerama mpaka nkhope yake pansi+ kenako anagona pansi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena