Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 25:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Kenako anthuwo anangoona mwamuna wina wachiisiraeli+ akubwera ndi mkazi wachimidiyani.+ Anali kubwera naye kufupi ndi abale ake, pamaso pa Mose ndi pamaso pa khamu lonse la ana a Isiraeli. Pa nthawiyi n’kuti Aisiraeliwo akulira pakhomo la chihema chokumanako.

  • 2 Samueli 12:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Iweyo unachita zinthu zimenezi mobisa,+ koma ine ndidzachita zimenezi pamaso pa Isiraeli+ yense, masanasana.’”+

  • Yesaya 3:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Maonekedwe a nkhope zawo akuwachitira umboni wotsutsana nawo,+ ndipo anthuwo akunena za tchimo lawo lofanana ndi la Sodomu.+ Iwo sanalibise. Tsoka kwa iwo, chifukwa adzibweretsera mavuto.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena