Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 49:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Yuda ndi mwana wa mkango.+ Umapha nyama n’kubwerako ndithu, mwana wanga. Iye amapinda mawondo ake n’kudziwongola ngati mkango utagona pansi. Ndipo monga mkango, ndani angamudzutse?+

  • Numeri 24:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Iye anagwada pansi. Anagona pansi ngati mkango.

      Ngati mkango, ndani angayese kum’dzutsa?+

      Odalitsa iwe n’ngodalitsika,+

      Ndipo otemberera iwe n’ngotembereredwa.”+

  • 2 Samueli 1:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Sauli ndi Yonatani,+ anthu okondeka ndi osangalatsa pamene anali ndi moyo,

      Ngakhale pa imfa yawo sanasiyane.+

      Iwo anali aliwiro kuposa chiwombankhanga,+

      Amphamvu kuposa mikango.+

  • Yesaya 31:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pakuti Yehova wandiuza kuti: “Mkango umalira moopseza, ngakhale mkango wamphamvu,+ poteteza nyama imene wagwira. Abusa ambirimbiri akaitanidwa kuti adzauthamangitse, ngakhale umve mawu awo suchita mantha ndipo ngakhale azichita phokoso suopa. M’njira yomweyo, Yehova wa makamu adzatsika kuti achite nkhondo poteteza phiri la Ziyoni ndiponso poteteza phiri lake laling’ono.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena