Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 5:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Davide anali ndi zaka 30 pamene anakhala mfumu. Iye analamulira monga mfumu kwa zaka 40.+

  • 1 Mafumu 2:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Davide analamulira Isiraeli zaka 40.+ Ku Heburoni+ analamulira zaka 7,+ ndipo ku Yerusalemu analamulira zaka 33.+

  • 1 Mbiri 23:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Davide anali atakalamba+ ndiponso atakhutira ndi masiku a moyo wake. Chotero analonga mwana wake Solomo+ kukhala mfumu ya Isiraeli.

  • 1 Mbiri 29:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Masiku onse amene iye analamulira Isiraeli anakwana zaka 40.+ Ku Heburoni analamulira zaka 7,+ ndipo ku Yerusalemu analamulira zaka 33.+

  • Salimo 90:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Masiku a moyo wathu amangokwana zaka 70,+

      Ndipo ngati tili ndi mphamvu yapadera amakwana zaka 80.+

      Koma ngakhale zili choncho, amangodzaza ndi mavuto ndi zopweteka.+

      Pakuti masiku amene timakhala ndi moyo amatha mwamsanga ndipo timachoka mofulumira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena