Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 25:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 “‘Choncho musamagulitsiretu malo anu mpaka kalekale+ chifukwa dzikolo ndi langa.+ Kwa ine, inu ndinu alendo m’dziko langa.+

  • Numeri 36:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Cholowa cha ana a Isiraeli chisachoke ku fuko lina kupita ku fuko lina. Aliyense wa ana a Isiraeli ayenera kusunga cholowa cha fuko la makolo ake.

  • Ezekieli 46:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Mtsogoleri wa anthu asamatenge cholowa chilichonse cha anthu ndi kuwakakamiza kuchoka m’malo awo.+ Ana ake aamuna aziwapatsa cholowa kuchokera pamalo amene ali nawo, kuti anthu anga asamwazikane ndi kuchoka m’malo awo.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena