Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 25:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Muyezo wako woyezera kulemera kwa chinthu uzikhala wolondola ndi woyenera. Muyezo wako wa efa uzikhala wolondola ndi woyenera kuti masiku ako achuluke m’dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa.+

  • Salimo 21:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Mfumuyo inakupemphani moyo. Ndipo munaipatsadi,+

      Munaipatsa masiku ochuluka kuti ikhale mpaka kalekale, ndithu mpaka muyaya.+

  • Salimo 91:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndidzamukhutiritsa ndi masiku ambiri,+

      Ndipo ndidzamuonetsa chipulumutso changa.”+

  • Miyambo 3:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Masiku ochuluka ali m’dzanja lake lamanja.+ M’dzanja lake lamanzere muli chuma ndi ulemerero.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena