Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 7:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 M’kupita kwa nthawi Hiramu+ anapanga mabeseni,+ mafosholo+ ndi mbale zolowa.+ Kenako iye anamaliza+ ntchito yonse imene anali kugwirira Mfumu Solomo, yokhudza nyumba ya Yehova.

  • 2 Mbiri 2:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Tsopano ndikutumiza munthu waluso ndi wozindikira, dzina lake Hiramu-abi.+

  • 2 Mbiri 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pomalizira pake Hiramu anapanga ndowa,+ mafosholo+ ndi mbale zolowa.+

      Chotero iye anamaliza ntchito imene anali kugwirira Mfumu Solomo pa nyumba ya Mulungu woona.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena