Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 10:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Panali masitepe 6 okafika kumpando wachifumuwo. Kuseri kwa mpando wachifumuwo kunali chotchingira chozungulira. Mpandowo unali ndi moika manja mbali zonse ziwiri. M’mphepete mwake munali zifaniziro ziwiri za mikango+ itaimirira.+

  • 2 Mbiri 9:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Pamasitepe 6 amenewo, panali zifaniziro 12 za mikango+ itaimirira, mbali iyi ndi iyi. Panalibenso ufumu wina umene unali ndi mpando wachifumu ngati umenewo.+

  • Ezekieli 41:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Nkhope ya munthu inayang’ana chithunzi cha mtengo wa kanjedza kumbali iyi ndipo nkhope ya mkango wamphamvu inayang’ana mtengo wa kanjedza kumbali inayo.+ Zithunzi zimenezi zinali zojambula pakhoma mochita kugoba ndipo zinajambulidwa kuzungulira m’nyumba monsemo.

  • Hoseya 5:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ine ndidzakhala ngati mkango wamphamvu kwa Efuraimu+ ndiponso ngati mkango wamphongo kwa nyumba ya Yuda. Ineyo ndidzawakhadzulakhadzula ndekha ndi kuwataya ndipo sipadzakhala wowalanditsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena