3 “Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa wanena kuti, ‘Mzinda umene unali kupita kukamenya nkhondo ndi anthu 1,000 udzatsala ndi anthu 100, ndipo mzinda umene unali kupita kukamenya nkhondo ndi anthu 100 udzatsala ndi anthu 10. Zimenezi ndi zimene zidzachitikira nyumba ya Isiraeli.’+