Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 19:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Iweyo wamva zimene mafumu a Asuri anachita kumayiko onse amene anawawononga.+ Ndiye kodi iweyo ukuona ngati upulumuka?+

  • Yesaya 8:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 popeza mwanayo asanadziwe kuitana+ kuti, ‘Ababa!’ kapena ‘Amama!’ anthu adzanyamula chuma cha ku Damasiko ndi katundu wolandidwa ku Samariya n’kupita naye pamaso pa mfumu ya Asuri.”+

  • Hoseya 8:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Iwo apita kudziko la Asuri+ ngati mbidzi yoyenda yokha.+ Koma Efuraimu walipira akazi kuti azigona nawo.+

  • Amosi 5:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 “Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa wanena kuti, ‘Mzinda umene unali kupita kukamenya nkhondo ndi anthu 1,000 udzatsala ndi anthu 100, ndipo mzinda umene unali kupita kukamenya nkhondo ndi anthu 100 udzatsala ndi anthu 10. Zimenezi ndi zimene zidzachitikira nyumba ya Isiraeli.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena