2 Mafumu 19:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 “Amuna inu mukamuuze Hezekiya mfumu ya Yuda kuti, ‘Usalole Mulungu wako amene ukum’dalira kuti akunamize,+ ponena kuti: “Yerusalemu+ saperekedwa m’manja mwa mfumu ya Asuri.”+ 2 Mbiri 32:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 “Senakeribu mfumu ya Asuri yanena kuti,+ ‘Kodi mukudalira chiyani poti mukungokhala mosatekeseka, Yerusalemu atazunguliridwa?+ Salimo 4:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Inu ana a anthu, kodi mudzandinyoza chifukwa cha ulemerero wanga+ kufikira liti?Mudzakonda zinthu zopanda pake kufikira liti?Mudzafunafuna nkhani yoti mundinamizire kufikira liti? [Seʹlah.] Yesaya 36:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Ngati inu mungandiuze kuti, ‘Tikudalira Yehova Mulungu wathu,’ kodi si iye amene Hezekiya wamuchotsera malo ake okwezeka+ ndi maguwa ake ansembe,+ n’kuuza Yuda ndi Yerusalemu kuti, ‘Muzigwada pamaso pa guwa lansembe ili’?”’+ Yesaya 37:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 “Amuna inu mukamuuze Hezekiya mfumu ya Yuda kuti, ‘Usalole Mulungu wako amene ukumudalira kuti akunamize,+ ponena kuti: “Yerusalemu saperekedwa m’manja mwa mfumu ya Asuri.”+
10 “Amuna inu mukamuuze Hezekiya mfumu ya Yuda kuti, ‘Usalole Mulungu wako amene ukum’dalira kuti akunamize,+ ponena kuti: “Yerusalemu+ saperekedwa m’manja mwa mfumu ya Asuri.”+
10 “Senakeribu mfumu ya Asuri yanena kuti,+ ‘Kodi mukudalira chiyani poti mukungokhala mosatekeseka, Yerusalemu atazunguliridwa?+
2 Inu ana a anthu, kodi mudzandinyoza chifukwa cha ulemerero wanga+ kufikira liti?Mudzakonda zinthu zopanda pake kufikira liti?Mudzafunafuna nkhani yoti mundinamizire kufikira liti? [Seʹlah.]
7 Ngati inu mungandiuze kuti, ‘Tikudalira Yehova Mulungu wathu,’ kodi si iye amene Hezekiya wamuchotsera malo ake okwezeka+ ndi maguwa ake ansembe,+ n’kuuza Yuda ndi Yerusalemu kuti, ‘Muzigwada pamaso pa guwa lansembe ili’?”’+
10 “Amuna inu mukamuuze Hezekiya mfumu ya Yuda kuti, ‘Usalole Mulungu wako amene ukumudalira kuti akunamize,+ ponena kuti: “Yerusalemu saperekedwa m’manja mwa mfumu ya Asuri.”+