Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 18:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Choncho Rabisake+ anawauza kuti: “Mukauze Hezekiya kuti, ‘Mfumu yaikulu,+ mfumu ya Asuri yanena kuti: “Kodi ukudalira chiyani?+

  • 2 Mafumu 19:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Kodi ndani amene iwe wamutonza+ ndi kumulankhula monyoza?+

      Ndipo ndani amene iwe wam’kwezera mawu,+

      Ndi kum’kwezera maso ako m’mwamba?+

      Ndi Woyera wa Isiraeli!+

  • Salimo 11:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ine ndathawira kwa Yehova.+

      Kodi mulibe mantha? Mukundiuza kuti:

      “Thawirani kumapiri anu ngati mbalame!+

  • Salimo 22:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 “Anadzipereka kwa Yehova.+ Amupulumutse Iyeyo!+

      Ngati Mulungu amamukonda, amulanditse!”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena