Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 20:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Usakhale ndi milungu ina iliyonse+ kupatulapo ine.*

  • Deuteronomo 32:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Iwo anali kupereka nsembe kwa ziwanda, osati kwa Mulungu.+

      Anapereka nsembe kwa milungu imene sanaidziwe,+

      Milungu yatsopano yongobwera kumene,+

      Imene makolo anu akale sanaidziwe.

  • Oweruza 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Iwo anasiya Yehova, Mulungu wa makolo awo amene anawatulutsa m’dziko la Iguputo,+ n’kuyamba kutsatira milungu ina mwa milungu ya anthu owazungulira.+ Anayamba kugwadira milungu imeneyo, moti anakhumudwitsa Yehova.+

  • 1 Mafumu 9:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Koma inuyo ndi ana anu mukadzabwerera n’kusiya kunditsatira,+ osasunga malamulo anga amene ndakupatsani, komanso mukadzapita kukatumikira milungu ina+ ndi kuigwadira,

  • Salimo 106:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Anayamba kutumikira mafano awo,+

      Ndipo mafanowo anakhala msampha wawo.+

  • Yeremiya 2:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kodi pali mtundu wa anthu umene unasinthanitsapo milungu yawo+ ndi zinthu zimene kwa iwo si milungu yeniyeni?+ Koma anthu anga asinthanitsa ulemerero wanga ndi zinthu zosapindulitsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena