Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Pakuti Yehova adzaweruza anthu ake,+

      Ndipo adzamva chisoni chifukwa cha atumiki ake,+

      Chifukwa adzaona kuti thandizo lawachokera.

      Adzaona kuti pangokhala munthu wonyozeka ndi wopanda pake.

  • Oweruza 5:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mawu a anthu ena otunga madzi anamveka pamalo otungira madzi,+

      Kumeneko anayamba kusimba ntchito zolungama za Yehova,+

      Anasimba ntchito zolungama za anthu ake okhala m’midzi ya Isiraeli.

      Atatero m’pamene anthu a Yehova anapita kumizinda.

  • 2 Mafumu 7:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Chotero zinachitikadi monga mmene munthu wa Mulungu woona uja ananenera kwa mfumu, kuti: “Balere wokwana miyezo iwiri ya seya mtengo wake udzafika pa sekeli imodzi, ndipo ufa wosalala wokwana muyezo umodzi wa seya, mtengo wake udzafikanso pa sekeli imodzi mawa, pa nthawi ngati ino pachipata cha Samariya.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena