Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 22:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Anapitiriza kubisidwa m’nyumba ya Mulungu woona zaka 6,+ pamene Ataliya+ anali mfumukazi ya dzikolo.+

  • Salimo 12:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Anthu oipa akuyendayenda ponseponse,

      Chifukwa ana a anthu amayamikira zoipa.+

  • Yesaya 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Amene amagawira anthu anga ntchito, akuwagwiritsa ntchito mwankhanza, ndipo akazi ndi amene akuwalamulira.+ Inu anthu anga, amene akukutsogolerani akukusocheretsani,+ ndipo asokoneza njira yanu.+

  • Malaki 3:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Panopa anthu odzikuza tikuwatcha odala.+ Komanso anthu ochita zoipa zinthu zikuwayendera bwino.+ Iwo ayesa Mulungu koma sakulandira chilango.’”+

  • 1 Timoteyo 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Sindikuvomereza kuti mkazi aziphunzitsa+ kapena kukhala ndi ulamuliro pa mwamuna,+ koma azikhala chete.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena