2 Samueli 22:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Davide analankhula ndi Yehova mawu a nyimbo iyi,+ pa tsiku limene Yehova anamulanditsa kwa adani ake+ onse ndiponso m’manja mwa Sauli.+ 2 Samueli 23:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Mawu omaliza amene Davide ananena ndi awa:+“Mawu a Davide mwana wa Jese,+Mawu a munthu wamphamvu amene anakwezedwa pamwamba,+Wodzozedwa+ wa Mulungu wa Yakobo,Munthu wosangalatsa wotchulidwa m’nyimbo zokoma+ za Isiraeli. 1 Mbiri 16:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Ndiyeno Davide anaika Alevi+ ena kukhala otumikira+ pa likasa la Yehova kuti azikumbutsa+ anthu, kuyamika,+ ndi kutamanda+ Yehova Mulungu wa Isiraeli. 2 Akorinto 9:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Zili choncho chifukwa utumiki wothandiza anthu umenewu si kuti ukungopatsa oyerawo zinthu zochuluka zimene akufunikira,+ koma ukuchititsanso anthu ambiri kupereka mapemphero ochuluka oyamika Mulungu.
22 Davide analankhula ndi Yehova mawu a nyimbo iyi,+ pa tsiku limene Yehova anamulanditsa kwa adani ake+ onse ndiponso m’manja mwa Sauli.+
23 Mawu omaliza amene Davide ananena ndi awa:+“Mawu a Davide mwana wa Jese,+Mawu a munthu wamphamvu amene anakwezedwa pamwamba,+Wodzozedwa+ wa Mulungu wa Yakobo,Munthu wosangalatsa wotchulidwa m’nyimbo zokoma+ za Isiraeli.
4 Ndiyeno Davide anaika Alevi+ ena kukhala otumikira+ pa likasa la Yehova kuti azikumbutsa+ anthu, kuyamika,+ ndi kutamanda+ Yehova Mulungu wa Isiraeli.
12 Zili choncho chifukwa utumiki wothandiza anthu umenewu si kuti ukungopatsa oyerawo zinthu zochuluka zimene akufunikira,+ koma ukuchititsanso anthu ambiri kupereka mapemphero ochuluka oyamika Mulungu.