Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 149:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 149 Tamandani Ya, anthu inu!+

      Imbirani Yehova nyimbo yatsopano,+

      Muimbireni nyimbo zomutamanda mu mpingo wa anthu ake okhulupirika.+

  • Yesaya 43:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 ndiponso kuti anthu amene ndinawapanga kuti akhale anga, anene za ulemerero wanga.+

  • Akolose 3:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Mawu a Khristu akhazikike mwa inu ndipo akupatseni nzeru zonse.+ Pitirizani kuphunzitsana+ ndi kulangizana mwa masalimo,+ nyimbo zotamanda Mulungu, ndi nyimbo zauzimu+ zogwira mtima. Pitirizani kuimbira Yehova+ m’mitima yanu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena