Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 3:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Iwo anayamba kuimba molandizana potamanda+ ndi kuthokoza Yehova kuti, “iye ndi wabwino,+ pakuti kukoma mtima kosatha kumene amakusonyeza kwa Isiraeli kudzakhala mpaka kalekale.”*+ Ndipo anthu onse anafuula mokweza kwambiri+ potamanda Yehova chifukwa cha kumangidwa kwa maziko a nyumba ya Yehova.

  • Salimo 86:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma inu Yehova, ndinu Mulungu wachifundo ndi wachisomo,+

      Wosakwiya msanga+ ndiponso wodzaza ndi kukoma mtima kosatha ndi choonadi.+

  • Salimo 103:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Koma Yehova adzapitiriza kusonyeza kukoma mtima kwake kosatha mpaka kalekale,+

      Kwa anthu amene amamuopa.+

      Ndipo adzapitiriza kusonyeza chilungamo chake kwa ana a ana awo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena