1 Samueli 22:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Chotero iye anawasiya m’manja mwa mfumu ya Mowabu, moti iwo anapitiriza kukhala kumeneko masiku onse amene Davide anakhala m’malo ovuta kufikako.+ 1 Samueli 23:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Tsopano Davide anayamba kukhala m’chipululu, m’malo ovuta kufikako. Iye anapitiriza kukhala m’dera lamapiri m’chipululu cha Zifi,+ ndipo Sauli anali kumufunafuna nthawi zonse,+ koma Mulungu sanam’pereke m’manja mwake.+ 1 Samueli 24:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Zitatero, Davide analumbirira Sauli. Kenako Sauliyo anapita kwawo,+ koma Davide ndi amuna amene anali kuyenda naye anapita kumalo ovuta kufikako.+
4 Chotero iye anawasiya m’manja mwa mfumu ya Mowabu, moti iwo anapitiriza kukhala kumeneko masiku onse amene Davide anakhala m’malo ovuta kufikako.+
14 Tsopano Davide anayamba kukhala m’chipululu, m’malo ovuta kufikako. Iye anapitiriza kukhala m’dera lamapiri m’chipululu cha Zifi,+ ndipo Sauli anali kumufunafuna nthawi zonse,+ koma Mulungu sanam’pereke m’manja mwake.+
22 Zitatero, Davide analumbirira Sauli. Kenako Sauliyo anapita kwawo,+ koma Davide ndi amuna amene anali kuyenda naye anapita kumalo ovuta kufikako.+