Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 15:55
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 55 Maoni,+ Karimeli, Zifi,+ Yuta,

  • 1 Samueli 23:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Chotero iwo ananyamuka ndi kupita ku Zifi,+ Sauli atamusiya kumbuyo. Izi zinachitika pamene Davide ndi amuna amene anali kuyenda naye anali m’chipululu cha Maoni,+ mu Araba,+ kum’mwera kwa Yesimoni.

  • 1 Samueli 26:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Patapita nthawi, amuna a ku Zifi+ anapita kwa Sauli ku Gibeya,+ ndipo anamuuza kuti: “Kodi simukudziwa kuti Davide akubisala kuphiri la Hakila+ moyang’anana ndi Yesimoni?”*+

  • 1 Mbiri 2:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Ana a Kalebe+ m’bale wake wa Yerameeli anali Mesa mwana wake woyamba, yemwe anali bambo wa Zifi, ndi ana a Maresha bambo wa Heburoni.

  • Salimo 54:kam
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • Kwa wotsogolera nyimbo: Nyimboyi iimbidwe ndi zipangizo za zingwe. Masikili.* Salimo la Davide. Pa nthawi imene Zifi anabwera kudzauza Sauli kuti: “Kodi simukudziwa kuti Davide akubisala kwathu?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena