19 Kenako amuna a ku Zifi+ anapita kwa Sauli ku Gibeya+ kukamuuza kuti: “Kodi Davide si uyu akubisala+ pafupi ndi ife m’malo ovuta kufikamo ku Horesi,+ paphiri la Hakila+ limene lili kudzanja lamanja* la Yesimoni?*+
26Patapita nthawi, amuna a ku Zifi+ anapita kwa Sauli ku Gibeya,+ ndipo anamuuza kuti: “Kodi simukudziwa kuti Davide akubisala kuphiri la Hakila+ moyang’anana ndi Yesimoni?”*+