Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 14:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Usiku iye anagawa m’magulu asilikali akewo,+ omwe anali akapolo ake, kuti amenyane ndi adaniwo. Ndipo anawagonjetsa, moti anawapitikitsa mpaka ku Hoba, kumpoto kwa Damasiko.

  • 2 Samueli 8:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Kenako Davide anamanga midzi ya asilikali+ m’dera la Asiriya a ku Damasiko ndipo Asiriyawo anakhala akapolo a Davide moti anali kukhoma msonkho+ kwa iye. Yehova anapitiriza kupulumutsa Davide kulikonse kumene wapita.+

  • 1 Mbiri 18:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pamene Asiriya a ku Damasiko anabwera kudzathandiza Hadadezeri mfumu ya Zoba,+ Davide anapha amuna 22,000 a ku Siriya.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena