21Tsopano mfumu ya Akanani ya ku Aradi+ yomwe inali kukhala ku Negebu,+ inamva kuti Aisiraeli akubwera kudzera njira ya ku Atarimu. Itamva zimenezo inapita kukamenyana nawo ndipo Aisiraeli ena inawagwira ndi kupita nawo kudziko lake.
7 Kenako anafika kumzinda wa mpanda wolimba wa Turo+ ndiponso kumizinda yonse ya Ahivi+ ndi Akanani. Pamapeto pake anafika ku Beere-seba+ ku Negebu,+ m’dziko la Yuda.