Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 49:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 “Benjamini adzapitiriza kukhadzula ngati mmbulu.+ M’mawa adzadya nyama imene wagwira, ndipo madzulo adzagawa zimene wafunkha.”+

  • 1 Samueli 9:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Pamenepo Sauli anayankha kuti: “Kodi ine si wa m’fuko la Benjamini, fuko laling’ono kwambiri+ pa mafuko onse a Isiraeli?+ Ndipo kodi banja langa sindilo laling’ono kwambiri pa mabanja onse a m’fuko la Benjamini?+ Ndiye n’chifukwa chiyani mwalankhula mawu otere kwa ine?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena