Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 4:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 n’cholinga choti mufufuze m’buku la mbiri+ ya makolo anu. Mukafufuza m’bukulo mupeza kuti mzinda umenewu ndi mzinda woukira ndi wowonongetsa chuma cha mafumu ndi zigawo za mayiko. Mupezanso kuti mumzinda umenewu mwakhala muli anthu oyambitsa kupanduka kuyambira kalekale. N’chifukwa chake mzindawu uli bwinja.+

  • Esitere 6:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Usiku umenewo mfumu inasowa tulo.+ Choncho inaitanitsa buku limene anali kulembamo zochitika+ za m’masiku amenewo. Ndiyeno anawerenga zochitikazo pamaso pa mfumu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena