-
Mateyu 25:44Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
44 Pamenepo nawonso adzayankha kuti, ‘Ambuye, tinakuonani liti muli wanjala kapena waludzu kapena mlendo kapena wamaliseche kapena mukudwala kapena muli m’ndende ife osakutumikirani?’
-