Yobu 10:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Ndisanapite. Ndikapita sindibweranso,+Ndikapita kudziko lamdima wandiweyani,+ Yobu 14:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Anthu nawonso amagona pansi osadzuka.+Sadzadzuka mpaka kumwamba kutachoka,+Sadzadzutsidwa ku tulo tawo.+ Salimo 78:39 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 39 Iye anali kukumbukira nthawi zonse kuti iwo ndi anthu athupi la nyama,+Anali kukumbukira kuti moyo wawo umachoka ndipo subwereranso.+ Mlaliki 9:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Chilichonse chimene dzanja lako lapeza kuti lichite, uchichite ndi mphamvu zako zonse,+ pakuti kulibe kugwira ntchito, kuganiza zochita, kudziwa zinthu,+ kapena nzeru,+ ku Manda*+ kumene ukupitako.+
21 Ndisanapite. Ndikapita sindibweranso,+Ndikapita kudziko lamdima wandiweyani,+ Yobu 14:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Anthu nawonso amagona pansi osadzuka.+Sadzadzuka mpaka kumwamba kutachoka,+Sadzadzutsidwa ku tulo tawo.+ Salimo 78:39 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 39 Iye anali kukumbukira nthawi zonse kuti iwo ndi anthu athupi la nyama,+Anali kukumbukira kuti moyo wawo umachoka ndipo subwereranso.+ Mlaliki 9:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Chilichonse chimene dzanja lako lapeza kuti lichite, uchichite ndi mphamvu zako zonse,+ pakuti kulibe kugwira ntchito, kuganiza zochita, kudziwa zinthu,+ kapena nzeru,+ ku Manda*+ kumene ukupitako.+
12 Anthu nawonso amagona pansi osadzuka.+Sadzadzuka mpaka kumwamba kutachoka,+Sadzadzutsidwa ku tulo tawo.+
39 Iye anali kukumbukira nthawi zonse kuti iwo ndi anthu athupi la nyama,+Anali kukumbukira kuti moyo wawo umachoka ndipo subwereranso.+
10 Chilichonse chimene dzanja lako lapeza kuti lichite, uchichite ndi mphamvu zako zonse,+ pakuti kulibe kugwira ntchito, kuganiza zochita, kudziwa zinthu,+ kapena nzeru,+ ku Manda*+ kumene ukupitako.+