Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 35:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Iwo amangokhalira kulirira thandizo, koma iye sawayankha+

      Chifukwa cha kunyada+ kwa anthu oipa.

  • Salimo 18:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Adzafuula kupempha thandizo, koma sipadzapezeka wowapulumutsa,+

      Adzafuulira Yehova, koma sadzawayankha.+

  • Miyambo 28:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Munthu amene amathawitsa khutu lake kuti asamve chilamulo,+ ngakhale pemphero lake limakhala lonyansa.+

  • Yeremiya 11:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Choncho Yehova wanena kuti, ‘Ndiwagwetsera tsoka+ limene sadzatha kulithawa.+ Iwo adzandiitana kuti ndiwathandize, koma sindidzawamvera.+

  • Yakobo 4:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mumapempha koma simulandira, chifukwa mukupempha ndi cholinga choipa,+ kuti mukhutiritse zilakolako za matupi anu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena