Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 18:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Adzafuula kupempha thandizo, koma sipadzapezeka wowapulumutsa,+

      Adzafuulira Yehova, koma sadzawayankha.+

  • Miyambo 1:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Pa nthawi imeneyo azidzangondiitana koma sindidzayankha.+ Adzakhalira kundifunafuna koma sadzandipeza,+

  • Yesaya 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mukatambasula manja anu,+ ndimakubisirani maso anga.+ Ngakhale mupereke mapemphero ambiri,+ ine sindimvetsera.+ Manja anu adzaza magazi amene mwakhetsa.+

  • Yeremiya 14:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pamene akusala kudya ine sindikumvetsera kuchonderera kwawo.+ Pamene akupereka nsembe zopsereza zathunthu ndi nsembe zambewu ine sindikukondwera nazo,+ ndipo ndiwawononga ndi lupanga, njala yaikulu ndiponso mliri.”+

  • Ezekieli 8:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Choncho ineyo ndidzachitapo kanthu mwaukali.+ Diso langa silidzawamvera chisoni ndipo sindidzawachitira chifundo.+ Iwo adzandiitana mofuula, koma ine sindidzamva.”+

  • Mika 3:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pa nthawiyo adzafuulira Yehova kuti awathandize, koma sadzawayankha.+ Adzawabisira nkhope yake pa nthawi imeneyo+ chifukwa cha zoipa zimene anali kuchita.+

  • Zekariya 7:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 “‘Popeza kuti ine ndikawaitana sanali kundimvera,+ iwonso akandiitana sindinali kuwamvera,’+ watero Yehova wa makamu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena