Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 9:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Pa tsiku la 24 la mwezi umenewu+ ana a Isiraeli anasonkhana pamodzi. Iwo anali kusala kudya+ atavala ziguduli*+ ndiponso atadzithira dothi+ kumutu.

  • Maliro 2:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Akuluakulu a mwana wamkazi wa Ziyoni akhala pansi ndipo akhala chete.+

      Iwo athira fumbi pamitu+ yawo ndipo avala ziguduli.*+

      Anamwali a Yerusalemu aweramitsa mitu yawo mpaka padothi.+

  • Ezekieli 27:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Iwo adzakulirira mofuula ndi mowawidwa mtima.+ Adzadzithira dothi kumutu+ ndi kugubuduzika paphulusa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena