Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 9:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Pa tsiku la 24 la mwezi umenewu+ ana a Isiraeli anasonkhana pamodzi. Iwo anali kusala kudya+ atavala ziguduli*+ ndiponso atadzithira dothi+ kumutu.

  • Yobu 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Atakweza maso awo ali chapatali, sanamuzindikire poyamba. Kenako anayamba kulira mokweza mawu ndipo aliyense anang’amba+ malaya ake akunja odula manja, n’kuwaza fumbi m’mwamba pamwamba pa mitu yawo.+

  • Chivumbulutso 18:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Iwo anathira fumbi pamitu pawo+ akufuula, kulira ndi kumva chisoni,+ ndipo anati, ‘Kalanga ine! Kalanga ine! Mzinda waukuluwu, umene unalemeretsa+ onse okhala ndi ngalawa panyanja+ chifukwa cha chuma chake chamtengo wapatali, pakuti mu ola limodzi, wawonongedwa.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena