Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 9:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 N’chifukwa chake ndikunena kuti zonsezo mfundo yake ndi imodzi, yakuti:

      ‘Iye amapha osalakwa komanso oipa.’+

  • Yobu 35:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Mwanena kuti, ‘Kodi kulungamako n’kwantchito yanji kwa inu?+

      Kodi kundipindulitsa chiyani kuposa chimene ndikanapindula pochimwa?’+

  • Malaki 3:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “Inu mwanena kuti, ‘Kutumikira Mulungu n’kopanda phindu.+ Tapindulanji chifukwa chomutumikira ndiponso chifukwa choyenda mwachisoni pamaso pa Yehova wa makamu?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena