Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 14:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ndiyeno pa nthawi ya ulonda wam’mawa,* Yehova ali mumtambo ndi moto woima njo ngati chipilala,+ anayang’ana gulu la Aiguputo, ndipo anachititsa Aiguputowo kusokonezeka.+

  • Salimo 30:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Chifukwa mkwiyo wa Mulungu sukhalitsa pa munthu,+

      Koma kukoma mtima kwake ndi kwa moyo wonse.+

      Usiku kumakhala kulira,+ koma m’mawa kumakhala kufuula ndi chisangalalo.+

  • Salimo 143:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 M’mawa ndichititseni kumva za kukoma mtima kwanu kosatha,+

      Pakuti ndimadalira inu.+

      Ndidziwitseni njira imene ndiyenera kuyendamo,+

      Pakuti ndapereka moyo wanga kwa inu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena