Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 32:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Limbani mtima ndipo muchite zinthu mwamphamvu.+ Musaope+ kapena kuchita mantha+ ndi mfumu ya Asuri+ ndi khamu lalikulu limene ili nalo,+ chifukwa ife tili ndi ambiri kuposa amene ali ndi mfumuyo.

  • Salimo 3:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Sindidzaopa anthu masauzande makumimakumi

      Amene andiukira ndi kundizungulira.+

  • Salimo 118:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Inandizungulira ngati njuchi,+

      Koma inazima ngati moto wa zitsamba zaminga.+

      Ndinali kuikankhira kutali m’dzina la Yehova.+

  • Mateyu 26:47
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 Mawu adakali m’kamwa, Yudasi,+ mmodzi wa ophunzira 12 aja, anafika limodzi ndi khamu lalikulu la anthu kuchokera kwa ansembe aakulu ndi kwa akulu, atanyamula malupanga+ ndi zibonga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena