Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 40:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Inu Yehova, musasiye kundimvera chisoni.+

      Kukoma mtima kwanu kosatha komanso choonadi chanu zinditeteze nthawi zonse.+

  • Salimo 57:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Adzatumiza thandizo kuchokera kumwamba ndi kundipulumutsa.+

      Adzasokoneza wofuna kundiwakha ndi pakamwa pake.+ [Seʹlah.]

      Mulungu adzasonyeza kukoma mtima kwake kosatha ndi choonadi chake.+

  • Salimo 143:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Adani anga muwakhalitse chete monga mwa kukoma mtima kwanu kosatha.+

      Ndipo muwononge onse ondichitira zoipa,+

      Pakuti ine ndine mtumiki wanu.+

  • Miyambo 20:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Kukoma mtima kosatha ndiponso choonadi zimateteza mfumu,+ ndipo chifukwa cha kukoma mtima kosatha kumeneko mfumu imakhazikitsa mpando wake wachifumu.+

  • Mika 7:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Zonse zimene munanena kwa Yakobo zinali zoona ndipo Abulahamu munamusonyeza kukoma mtima kosatha. Ifenso mudzatichitira zomwezo chifukwa n’zimene munalonjeza makolo athu kalekale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena