Deuteronomo 15:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Samala kuti usalankhule mawu achabe mumtima mwako+ kuti, ‘Chaka cha 7, chaka choti anthu angongole amasuke chayandikira,’+ kuti usaolowere manja m’bale wako wosaukayo,+ osam’patsa kalikonse. Pamenepo iye adzafuulira Yehova chifukwa cha zimene iweyo wam’chitira+ ndipo udzapezeka kuti wachimwa.+ Yoswa 23:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 “Tsopano khalani olimba mtima kwambiri,+ kuti musunge ndi kuchita zonse zimene zinalembedwa m’buku+ la chilamulo cha Mose, posapatukira kudzanja lamanja kapena lamanzere.+ Salimo 40:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Wodala ndi munthu wamphamvu amene amakhulupirira Yehova,+Munthu amene sanacheukire anthu otsutsa,Kapena anthu amene anapatukira m’njira za mabodza.+
9 Samala kuti usalankhule mawu achabe mumtima mwako+ kuti, ‘Chaka cha 7, chaka choti anthu angongole amasuke chayandikira,’+ kuti usaolowere manja m’bale wako wosaukayo,+ osam’patsa kalikonse. Pamenepo iye adzafuulira Yehova chifukwa cha zimene iweyo wam’chitira+ ndipo udzapezeka kuti wachimwa.+
6 “Tsopano khalani olimba mtima kwambiri,+ kuti musunge ndi kuchita zonse zimene zinalembedwa m’buku+ la chilamulo cha Mose, posapatukira kudzanja lamanja kapena lamanzere.+
4 Wodala ndi munthu wamphamvu amene amakhulupirira Yehova,+Munthu amene sanacheukire anthu otsutsa,Kapena anthu amene anapatukira m’njira za mabodza.+